Genesis 46:12 - Buku Lopatulika12 Ndi ana aamuna a Yuda: Eri, ndi Onani, ndi Sela, ndi Perezi, ndi Zera; koma Eri ndi Onani anafa m'dziko la Kanani. Ndi ana aamuna a Perezi ndiwo Hezironi ndi Hamuli. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndi ana amuna a Yuda: Eri, ndi Onani, ndi Sela, ndi Perezi, ndi Zera; koma Eri ndi Onani anafa m'dziko la Kanani. Ndi ana amuna a Perezi ndiwo Hezironi ndi Hamuli. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ana a Yuda anali aŵa: Ere, Onani, Sela, Perezi ndi Zera, (koma Ere ndi Onani adaafera ku Kanani.) Ana a Perezi anali aŵa: Hezironi ndi Hamuli. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ana aamuna a Yuda ndi awa: Eri, Onani, Sela, Perezi ndi Zera. Koma Eri ndi Onani anamwalira mʼdziko la Kanaani. Ana a Perezi anali Hezironi ndi Hamuli. Onani mutuwo |