Genesis 46:13 - Buku Lopatulika13 Ndi ana aamuna a Isakara: Tola ndi Puva, ndi Iyobu, ndi Simironi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndi ana amuna a Isakara: Tola ndi Puva, ndi Iyobu, ndi Simironi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ana a Isakara anali aŵa: Tola, Puva, Iyobu ndi Simironi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ana aamuna a Isakara ndi awa: Tola, Puwa, Yobi ndi Simironi. Onani mutuwo |