Ndipo Yehova ananena ndi Mose m'chipululu cha Sinai, nati
Chauta adauza Mose m'chipululu cha Sinai kuti,
Yehova anawuza Mose mʼchipululu cha Sinai kuti,
Ana a Levi: Geresomo, Kohati, ndi Merari.
Mwezi wachitatu atatuluka ana a Israele m'dziko la Ejipito, tsiku lomwelo, analowa m'chipululu cha Sinai.
Koma Alevi monga mwa fuko la makolo ao sanawerengedwe mwa iwo.