Numeri 1:47 - Buku Lopatulika47 Koma Alevi monga mwa fuko la makolo ao sanawerengedwe mwa iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Koma Alevi monga mwa fuko la makolo ao sanawerengedwe mwa iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Alevi okha sadaŵaŵerengere kumodzi ndi enawo, potsata banja la makolo ao, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Koma mabanja a fuko la Levi okha sanawawerenge pamodzi ndi ena. Onani mutuwo |