Eksodo 19:1 - Buku Lopatulika1 Mwezi wachitatu atatuluka ana a Israele m'dziko la Ejipito, tsiku lomwelo, analowa m'chipululu cha Sinai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mwezi wachitatu atatuluka ana a Israele m'dziko la Ejipito, tsiku lomwelo, analowa m'chipululu cha Sinai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pa tsiku loyamba la mwezi wachitatu chichokere cha Aisraele ku Ejipito, mpamene adafika ku chipululu cha Sinai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ana a Israeli aja anafika ku chipululu cha Sinai pa tsiku loyamba la mwezi wachitatu chichokere mʼdziko la Igupto. Onani mutuwo |