Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 18:27 - Buku Lopatulika

27 Ndipo Mose analola mpongozi wake amuke; ndipo anachoka kunka ku dziko lake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndipo Mose analola mpongozi wake amuke; ndipo anachoka kunka ku dziko lake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Tsono Yeteroyo atalaŵirana naye Mose, adabwerera kwao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Kenaka Mose analola kuti mpongozi wake, Yetero anyamuke kubwerera ku dziko la kwawo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 18:27
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anamlola Rebeka mlongo wao ndi mlezi wake, amuke pamodzi ndi mnyamata wake wa Abrahamu, ndi anthu ake.


M'mamawa Labani anauka nampsompsona ana ake aamuna ndi aakazi, nawadalitsa: ndipo Labani anachoka, nabwera kumalo kwake.


Pamenepo munthuyo ananyamuka kuchoka, iye ndi mkazi wake wamng'ono ndi mnyamata wake; koma mpongozi wake, atate wa mkaziyo, ananena naye, Tapenya, lapendeka dzuwa, ugone kuno usiku; tapenya lapendekatu dzuwa, ugone kuno, nusekerere mtima wako; nimulawire mamawa kunka ulendo wanu kwanu.


Natuluka iye kumene anakhalako ndi apongozi ake awiri pamodzi naye; nanka ulendo wao kubwerera ku dziko la Yuda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa