Eksodo 18:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo anaweruza anthu nthawi zonse; mlandu wakuwakanika amabwera nao kwa Mose, ndi milandu yaing'ono yonse amaweruza okha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo anaweruza anthu nthawi zonse; mlandu wakuwakanika amabwera nao kwa Mose, ndi milandu yaing'ono yonse amaweruza okha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 ndipo iwowo ankaweruza anthu nthaŵi zonse. Milandu yovuta yokha ankabwera nayo kwa Mose, koma timilandu ting'onoting'ono ankangomaliza okha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Iwowa ankaweruza anthu nthawi zonse. Milandu yovuta ankabwera nayo kwa Mose, koma yosavuta ankayiweruza okha. Onani mutuwo |