Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 6:1 - Buku Lopatulika

1 Ana a Levi: Geresomo, Kohati, ndi Merari.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ana a Levi: Geresomo, Kohati, ndi Merari.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Ana a Levi naŵa: Geresomo, Kohati, ndi Merari.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ana a Levi anali awa: Geresoni, Kohati ndi Merari.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 6:1
10 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Levi: Geresoni, Kohati, ndi Merari.


Ndipo Davide anawagawa magawo monga mwa ana a Levi: Geresoni, Kohati, ndi Merari.


Ana a Levi: Geresomo, Kohati ndi Merari.


Ndi ana a Kohati: Amuramu, Izihara, ndi Hebroni, ndi Uziyele.


Wa Geresomo: Libini mwana wake, Yahati mwana wake, Zima mwana wake,


Ndipo monga munatikhalira dzanja lokoma la Mulungu wathu, anatitengera munthu wanzeru wa ana a Mali, mwana wa Levi, mwana wa Israele; ndi Serebiya, pamodzi ndi ana ake ndi abale ake khumi mphambu asanu ndi atatu;


Ndipo maina a ana aamuna a Levi, mwa kubadwa kwao ndiwo: Geresoni, ndi Kohati, ndi Merari; ndipo zaka za moyo wa Levi ndizo zana limodzi mphambu makumi atatu kudza zisanu ndi ziwiri.


Ndipo awa ndi owerengedwa ao a Alevi monga mwa mabanja ao: Geresoni, ndiye kholo la banja la Ageresoni; Kohati, ndiye kholo la banja la Akohati; Merari, ndiye kholo la banja la Amerari.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose m'chipululu cha Sinai, nati


Ndipo ana a Levi maina ao ndi awa: Geresoni, ndi Kohati ndi Merari.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa