Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 27:5 - Buku Lopatulika

Ndipo Mose anapita nao mlandu wao pamaso pa Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mose anapita nao mlandu wao pamaso pa Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mose adapita ndi mlandu umenewu pamaso pa Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono Mose anabweretsa nkhani yawo pamaso pa Yehova

Onani mutuwo



Numeri 27:5
12 Mawu Ofanana  

Ndikadalongosola mlandu wanga pamaso pake, ndikadadzaza m'kamwa mwanga ndi matsutsano.


Ndipo pomwepo ndidzakomana ndi iwe, ndi kulankhula ndi iwe, ndili pamwamba pa chotetezerapo, pakati pa akerubi awiriwo okhala pa likasa la mboni, zonse zimene ndidzakuuza za ana a Israele.


Ndipo anayamba wamsunga, popeza sichinanenedwe choyenera kumchitira iye.


Ndipo aime pamaso pa Eleazara wansembe, amene amfunsire monga mwa chiweruzo cha Urimu pamaso pa Yehova; ponena iye azituluka, ndi ponena iye azilowa, ndi iye ndi ana onse a Israele pamodzi naye, ndiwo khamu lonse.


Lichotsedwerenji dzina la atate wathu pakati pa banja lake, popeza alibe mwana wamwamuna? Tipatseni dziko lathulathu pakati pa abale a atate wathu.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


nati, Yehova analamulira mbuye wanga mupatse ana a Israele dzikoli mochita maere likhale cholowa chao; ndipo Yehova analamulira mbuye wathu mupatse ana ake aakazi cholowa cha Zelofehadi mbale wathu.


Ndipo Mose ananena nao, Baimani; ndimve chouza Yehova za inu.


Ndipo anayandikira pamaso pa Eleazara wansembe, ndi pamaso pa Yoswa mwana wa Nuni, ndi pamaso pa akalonga, ndi kuti, Yehova analamulira Mose atipatse cholowa pakati pa abale athu; chifukwa chake anawapatsa monga mwa lamulo la Yehova, cholowa pakati pa abale a atate wao.