Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 27:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Tsono Mose anabweretsa nkhani yawo pamaso pa Yehova

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

5 Ndipo Mose anapita nao mlandu wao pamaso pa Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo Mose anapita nao mlandu wao pamaso pa Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Mose adapita ndi mlandu umenewu pamaso pa Chauta.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 27:5
12 Mawu Ofanana  

Ndikanafotokoza mlandu wanga pamaso pake ndipo ndikanayankhula mawu odziteteza.


Ndizidzakumana nawe pamenepo, pamwamba pa chivundikiro cha bokosilo, pakati pa Akerubi awiriwo, ndikumadzakupatsa malamulo onse okhudzana ndi Aisraeli.


ndipo anamutsekera mʼndende chifukwa sankadziwa choti achite naye.


Ayime pamaso pa wansembe Eliezara, amene adzamudziwitse zimene Yehova akufuna pogwiritsa ntchito Urimu. Iye akalamula, Aisraeli onse azituluka ndipo akalamulanso, Aisraeliwo azibwereranso.”


Nʼchifukwa chiyani dzina la abambo athu lasowa pakati pa fuko lawo, kodi popeza analibe mwana wamwamuna? Tipatseni cholowa chathu pakati pa abale a abambo athu.”


ndipo Yehova anati kwa iye,


Iwo anati, “Pamene Yehova analamula mbuye wanga kuti apereke dziko ngati cholowa kwa Aisraeli mwa maere, anakulamulani inu kupereka cholowa cha mʼbale wathu Zelofehadi kwa ana ake aakazi.


Mose anawayankha kuti, “Dikirani mpaka nditamva zimene Yehova walamula zokhudza Inu.”


Iwo anapita kwa Eliezara wansembe, Yoswa mwana wa Nuni, ndi atsogoleri ndipo anati: “Yehova analamula Mose kuti ife ndi alongo athu atipatse cholowa chathu.” Choncho iwowo pamodzi ndi abale a abambo awo anawapatsa dera lina la dzikolo kuti likhale monga mwa lamulo la Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa