Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 11:6 - Buku Lopatulika

koma tsopano moyo wathu waphwa; tilibe kanthu pamaso pathu koma mana awa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

koma tsopano moyo wathu waphwa; tilibe kanthu pamaso pathu koma mana awa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma tsopano mphamvu zathu zatha, ndipo sitikuwona kanthu kena kakudya koma mana basi.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma tsopano chilakolako chathu chatha. Sitikuona kanthu kena kakudya koma mana basi!”

Onani mutuwo



Numeri 11:6
3 Mawu Ofanana  

Nanena naye, Iwe mwana wa mfumu, uonderanji tsiku ndi tsiku? Sungandiuze kodi? Ndipo Aminoni anati kwa iye, Ndikonda Tamara, mlongo wa mbale wanga Abisalomu.


Koma chilekere ife kufukizira mfumu yaikazi ya kumwamba, ndi kumthirira iye nsembe zothira, tasowa zonse, tathedwa ndi lupanga ndi njala.


Ndipo anthu ananena motsutsana ndi Mulungu, ndi Mose, ndi kuti, Mwatikwezeranji kutichotsa ku Ejipito kuti tifere m'chipululu? Pakuti mkate ndi madzi palibe, ndi mtima wathu walema nao mkate wachabe uwu.