Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 11:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Koma tsopano chilakolako chathu chatha. Sitikuona kanthu kena kakudya koma mana basi!”

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

6 koma tsopano moyo wathu waphwa; tilibe kanthu pamaso pathu koma mana awa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 koma tsopano moyo wathu waphwa; tilibe kanthu pamaso pathu koma mana awa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Koma tsopano mphamvu zathu zatha, ndipo sitikuwona kanthu kena kakudya koma mana basi.”

Onani mutuwo Koperani




Numeri 11:6
3 Mawu Ofanana  

Iye anafunsa Amnoni, “Nʼchifukwa chiyani iwe mwana wa mfumu, umaoneka wowonda mmawa uliwonse? Bwanji wosandiwuza?” Amnoni anamuyankha kuti, “Ine ndamukonda Tamara, mlongo wa mʼbale wanga Abisalomu.”


Koma kuchokera nthawi imene tinasiya kufukiza lubani ndi kupereka chopereka cha chakumwa kwa mfumukazi yakumwamba, ifeyo takhala tikusowa zinthu ndipo takhala tikuphedwa ndi lupanga ndi kufa ndi njala.”


ndipo anayankhula motsutsana ndi Mulungu ndi Mose, nati, “Chifukwa chiyani munatitulutsa kuchoka mʼdziko la Igupto kuti tidzafere mʼchipululu muno? Kuno kulibe chakudya, kulibe madzi ndipo chakudya cha chabechabechi tatopa nacho.”


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa