Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 11:34 - Buku Lopatulika

Ndipo anatcha malowo dzina lake Kibroti-Hatava; popeza pamenepo anaika anthu osusuka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anatcha malowo dzina lake Kibroti-Hatava; popeza pamenepo anaika anthu osusuka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nchifukwa chake malowo adaŵatcha Mandaankhuli, chifukwa choti kumeneko ndiko kumene adakwirira anthu ankhuli.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nʼchifukwa chake malowo anawatcha Kibiroti Hatava chifukwa pamenepo anakwirirapo anthu osusuka aja.

Onani mutuwo



Numeri 11:34
6 Mawu Ofanana  

pamenepo mkwiyo wa Mulungu unawaukira, ndipo anapha mwa onenepa ao, nagwetsa osankhika a Israele.


Kuchokera ku Kibroti-Hatava anthuwo anayenda kunka ku Hazeroti; nakhala ku Hazeroti.


Nachokera ku chipululu cha Sinai, nayenda namanga mu Kibroti-Hatava.


Nachokera ku Kibroti-Hatava, nayenda namanga mu Hazeroti.


Koma zinthu izi zinachitika, zikhale zotichenjeza ife, kuti tisalakalake zoipa ife, monganso iwowo analakalaka.


Ku Tabera, ndi ku Masa, ndi ku Kibroti-Hatava, munautsanso mkwiyo wa Yehova.