Masalimo 78:31 - Buku Lopatulika31 pamenepo mkwiyo wa Mulungu unawaukira, ndipo anapha mwa onenepa ao, nagwetsa osankhika a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 pamenepo mkwiyo wa Mulungu unawaukira, ndipo anapha mwa onenepa ao, nagwetsa osankhika a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 mkwiyo wa Mulungu udaŵayakira, ndipo adapha amphamvu onse pakati pao, adapha anyamata abwinoabwino onse a mu Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 mkwiyo wa Mulungu unawayakira; Iye anapha amphamvu onse pakati pawo, kugwetsa anyamata abwino kwambiri mu Israeli. Onani mutuwo |