Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:23 - Buku Lopatulika

Ndi pa gulu la fuko la ana a Manase anayang'anira Gamaliele mwana wa Pedazuri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi pa gulu la fuko la ana a Manase anayang'anira Gamaliele mwana wa Pedazuri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mtsogoleri wa gulu la fuko la Manase anali Gamaliele mwana wa Pedazuri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Gamalieli mwana wa Pedazuri ndiye anali mtsogoleri wa fuko la Manase.

Onani mutuwo



Numeri 10:23
4 Mawu Ofanana  

Wa ana a Yosefe: wa Efuremu, Elisama mwana wa Amihudi; wa Manase, Gamaliele mwana wa Pedazuri.


Ndipo anayenda a mbendera ya chigono cha ana a Efuremu, monga mwa magulu ao; ndi pa gulu lake anayang'anira Elisama mwana wa Amihudi.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Benjamini anayang'anira Abidani mwana wa Gideoni.


Tsiku lachisanu ndi chitatu kalonga wa ana a Manase ndiye Gamaliele mwana wa Pedazuri: