Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 10:23 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Gamalieli mwana wa Pedazuri ndiye anali mtsogoleri wa fuko la Manase.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

23 Ndi pa gulu la fuko la ana a Manase anayang'anira Gamaliele mwana wa Pedazuri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndi pa gulu la fuko la ana a Manase anayang'anira Gamaliele mwana wa Pedazuri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Mtsogoleri wa gulu la fuko la Manase anali Gamaliele mwana wa Pedazuri.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 10:23
4 Mawu Ofanana  

Mwa ana a Yosefe: kuchokera ku fuko la Efereimu, Elisama mwana wa Amihudi; kuchokera ku fuko la Manase, Gamalieli mwana wa Pedazuri;


Magulu a msasa wa Aefereimu anatsatira potsatira mbendera yawo. Elisama mwana wa Amihudi ndiye anali mtsogoleri wawo.


Abidani mwana wa Gideoni ndiye anali mtsogoleri wa mtundu wa Benjamini.


Pa tsiku lachisanu ndi chitatu Gamalieli mwana wa Pedazuri, mtsogoleri wa fuko Manase, anabweretsa chopereka chake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa