Numeri 1:10 - Buku Lopatulika10 Wa ana a Yosefe: wa Efuremu, Elisama mwana wa Amihudi; wa Manase, Gamaliele mwana wa Pedazuri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Wa ana a Yosefe: wa Efuremu, Elisama mwana wa Amihudi; wa Manase, Gamaliele mwana wa Pedazuri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Mwa ana a Yosefe: fuko la Efuremu, Elisama mwana wa Amihudi; fuko la Manase, Gamaliele mwana wa Pedazuri; Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mwa ana a Yosefe: kuchokera ku fuko la Efereimu, Elisama mwana wa Amihudi; kuchokera ku fuko la Manase, Gamalieli mwana wa Pedazuri; Onani mutuwo |