Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 1:11 - Buku Lopatulika

11 Wa Benjamini, Abidani mwana wa Gideoni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Wa Benjamini, Abidani mwana wa Gideoni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 fuko la Benjamini, Abidani mwana wa Gideoni;

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Abidani mwana wa Gideoni, kuchokera ku fuko la Benjamini,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:11
5 Mawu Ofanana  

Wa ana a Yosefe: wa Efuremu, Elisama mwana wa Amihudi; wa Manase, Gamaliele mwana wa Pedazuri.


Wa Dani, Ahiyezere mwana wa Amisadai.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Benjamini anayang'anira Abidani mwana wa Gideoni.


Ndi fuko la Benjamini: kalonga wa ana a Benjamini ndiye Abidani mwana wa Gideoni.


Tsiku lachisanu ndi chinai kalonga wa ana a Benjamini, ndiye Abidani mwana wa Gideoni:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa