Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 1:11 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Abidani mwana wa Gideoni, kuchokera ku fuko la Benjamini,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

11 Wa Benjamini, Abidani mwana wa Gideoni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Wa Benjamini, Abidani mwana wa Gideoni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 fuko la Benjamini, Abidani mwana wa Gideoni;

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:11
5 Mawu Ofanana  

Mwa ana a Yosefe: kuchokera ku fuko la Efereimu, Elisama mwana wa Amihudi; kuchokera ku fuko la Manase, Gamalieli mwana wa Pedazuri;


Ahiyezeri mwana wa Amisadai, kuchokera ku fuko la Dani,


Abidani mwana wa Gideoni ndiye anali mtsogoleri wa mtundu wa Benjamini.


Lotsatira lidzakhala fuko la Benjamini. Mtsogoleri wa Abenjamini ndi Abidani mwana wa Gideoni.


Pa tsiku lachisanu ndi chinayi Abidani mwana wa Gideoni mtsogoleri wa fuko la Benjamini, anabweretsa chopereka chake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa