Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 1:10 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Mwa ana a Yosefe: kuchokera ku fuko la Efereimu, Elisama mwana wa Amihudi; kuchokera ku fuko la Manase, Gamalieli mwana wa Pedazuri;

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

10 Wa ana a Yosefe: wa Efuremu, Elisama mwana wa Amihudi; wa Manase, Gamaliele mwana wa Pedazuri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Wa ana a Yosefe: wa Efuremu, Elisama mwana wa Amihudi; wa Manase, Gamaliele mwana wa Pedazuri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Mwa ana a Yosefe: fuko la Efuremu, Elisama mwana wa Amihudi; fuko la Manase, Gamaliele mwana wa Pedazuri;

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:10
8 Mawu Ofanana  

Abidani mwana wa Gideoni, kuchokera ku fuko la Benjamini,


Eliabu mwana wa Heloni, kuchokera ku fuko la Zebuloni,


Kumadzulo kudzakhala magulu a msasa wa Efereimu pamene pali mbendera yawo. Mtsogoleri wa Aefereimuwo ndi Elisama mwana wa Amihudi.


Fuko la Manase lidzakhala pafupi ndi Efereimu. Mtsogoleri wa Amanase ndi Gamalieli mwana wa Pedazuri.


Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri Elisama mwana wa Amihudi, mtsogoleri wa fuko la Efereimu, anabweretsa chopereka chake.


Pa tsiku lachisanu ndi chitatu Gamalieli mwana wa Pedazuri, mtsogoleri wa fuko Manase, anabweretsa chopereka chake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa