Numeri 7:54 - Buku Lopatulika54 Tsiku lachisanu ndi chitatu kalonga wa ana a Manase ndiye Gamaliele mwana wa Pedazuri: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201454 Tsiku lachisanu ndi chitatu kalonga wa ana a Manase ndiye Gamaliele mwana wa Pedazuri: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa54 Tsiku lachisanu ndi chitatu linali la Gamaliele mwana wa Pedazuri, mtsogoleri wa Amanase. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero54 Pa tsiku lachisanu ndi chitatu Gamalieli mwana wa Pedazuri, mtsogoleri wa fuko Manase, anabweretsa chopereka chake. Onani mutuwo |