Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 1:12 - Buku Lopatulika

Wa Dani, Ahiyezere mwana wa Amisadai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa Dani, Ahiyezere mwana wa Amisadai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

fuko la Dani, Ahiyezere mwana wa Amishadai;

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ahiyezeri mwana wa Amisadai, kuchokera ku fuko la Dani,

Onani mutuwo



Numeri 1:12
5 Mawu Ofanana  

Wa Benjamini, Abidani mwana wa Gideoni.


Wa Asere, Pagiyele mwana wa Okarani.


Pamenepo anayenda a mbendera ya chigono cha ana a Dani, ndiwo a m'mbuyombuyo a zigono zonse, monga mwa magulu ao; ndi pa gulu lake anayang'anira Ahiyezere mwana wa Amisadai.


Mbendera ya chigono cha Dani izikhala kumpoto monga mwa makamu ao; ndi kalonga wa ana a Dani ndiye Ahiyezere mwana wa Amisadai.


Tsiku lakhumi kalonga wa ana a Dani, ndiye Ahiyezere mwana wa Amisadai: