Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 7:66 - Buku Lopatulika

66 Tsiku lakhumi kalonga wa ana a Dani, ndiye Ahiyezere mwana wa Amisadai:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

66 Tsiku lakhumi kalonga wa ana a Dani, ndiye Ahiyezere mwana wa Amisadai:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

66 Tsiku lakhumi linali la Ahiyezere mwana wa Amishadai, mtsogoleri wa Adani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

66 Pa tsiku lakhumi Ahiyezeri mwana wa Amisadai, mtsogoleri wa fuko la Dani anabweretsa chopereka chake.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:66
2 Mawu Ofanana  

Wa Dani, Ahiyezere mwana wa Amisadai.


Mbendera ya chigono cha Dani izikhala kumpoto monga mwa makamu ao; ndi kalonga wa ana a Dani ndiye Ahiyezere mwana wa Amisadai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa