Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 7:65 - Buku Lopatulika

65 ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Abidani mwana wa Gideoni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

65 ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Abidani mwana wa Gideoni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

65 Ndipo zoperekera nsembe yachiyanjano zinali ng'ombe ziŵiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, ndi anaankhosa asanu amphongo a chaka chimodzi. Zimenezi ndizo zimene zinali zopereka za Abidani mwana wa Gideoni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

65 ngʼombe zazimuna ziwiri, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu, ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Abidani mwana wa Gideoni.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:65
3 Mawu Ofanana  

Wa Benjamini, Abidani mwana wa Gideoni.


Ndi fuko la Benjamini: kalonga wa ana a Benjamini ndiye Abidani mwana wa Gideoni.


mwa Iyenso kuyanjanitsa zinthu zonse kwa Iye mwini, atachita mtendere mwa mwazi wa mtanda wake; mwa Iyetu, kapena za padziko, kapena za mu Mwamba.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa