Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 1:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Ahiyezeri mwana wa Amisadai, kuchokera ku fuko la Dani,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

12 Wa Dani, Ahiyezere mwana wa Amisadai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Wa Dani, Ahiyezere mwana wa Amisadai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 fuko la Dani, Ahiyezere mwana wa Amishadai;

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:12
5 Mawu Ofanana  

Abidani mwana wa Gideoni, kuchokera ku fuko la Benjamini,


Pagieli mwana wa Okirani, kuchokera ku fuko la Aseri,


Pambuyo pa magulu onse panali magulu a msasa wa Dani, omwe ankateteza magulu onsewa ndipo ananyamuka potsatira mbendera yawo. Mtsogoleri wawo anali Ahiyezeri mwana wa Amisadai.


Kumpoto kudzakhala msasa wa magulu a Dani pamene pali mbendera yawo. Mtsogoleri wa Adani ndi Ahiyezeri mwana wa Amisadai.


Pa tsiku lakhumi Ahiyezeri mwana wa Amisadai, mtsogoleri wa fuko la Dani anabweretsa chopereka chake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa