Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 23:1 - Buku Lopatulika

Pomwepo Yesu analankhula ndi makamu a anthu ndi ophunzira ake,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pomwepo Yesu analankhula ndi makamu a anthu ndi ophunzira ake,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pambuyo pake Yesu adalankhula ndi gulu la anthu ochuluka pamodzi ndi ophunzira ake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo Yesu anati kwa magulu a anthu ndi ophunzira ake:

Onani mutuwo



Mateyu 23:1
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anadziitaniranso khamu la anthu, nanena nao, Mverani Ine nonsenu, ndipo dziwitsani:


Pomwepo pamene anthu a zikwizikwi a khamu anasonkhana pamodzi, kotero kuti anapondana, Iye anayamba kunena kwa ophunzira ake poyamba, Tachenjerani nokha ndi chotupitsa mikate cha Afarisi, chimene chili chinyengo.


Ndipo inunso, pa nokha mulekeranji kuweruza kolungama?