Mateyu 22:46 - Buku Lopatulika46 Ndipo sanalimbike mtima munthu aliyense kumfunsa kanthu kuyambira tsiku lomwelo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Ndipo sanalimbike mtima munthu aliyense kumfunsa kanthu kuyambira tsiku lomwelo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Panalibe ndi mmodzi yemwe wotha kumuyankha ngakhale mau amodzi. Tsono kuyambira tsiku limenelo panalibenso munthu amene adalimba mtima kuti amufunse mafunso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Panalibe wina anatha kuyankha, ndipo kuchokera pamenepo, panalibe wina anayerekeza kumufunsa funso. Onani mutuwo |