Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 20:3 - Buku Lopatulika

Ndipo anatuluka dzuwa litakwera, naona ena ataima chabe pabwalo;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anatuluka dzuwa litakwera, naona ena ataima chabe pabwalo;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa nthaŵi ya 9 koloko adapitanso, nakapeza ena atangokhala khale pa msika, osagwira ntchito.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Nthawi 9 koloko mmawa, anatulukanso naona ena atayimirira pa msika akungokhala.

Onani mutuwo



Mateyu 20:3
12 Mawu Ofanana  

Ulesi ugonetsa tulo tofa nato; ndipo moyo wamkhongono udzamva njala.


Taona, mphulupulu ya mng'ono wako Sodomu ndi iye, kudzikuza, kuchuluka kwa chakudya, ndi kupumula kwa mtambasali, anali nako iye ndi ana ake; ndipo sanalimbitse dzanja la wosauka ndi wosowa.


Ndipo pamene adapangana ndi antchito, pa rupiya latheka limodzi tsiku limodzi, anawatumiza kumunda wake.


ndipo kwa iwo anati, Pitani inunso kumunda, ndipo ndidzakupatsani chimene chili choyenera. Ndipo iwo anapita.


Ndipo panali ora lachitatu, ndipo anampachika Iye.


Koma pamene ambuye ake anaona kuti kulingalira kwa kupindula kwao kwatha, anagwira Paulo ndi Silasi, nawakokera kunka nao kubwalo kwa akulu,


Pakuti awa sanaledzere monga muyesa inu; pakuti ndi ora lachitatu lokha la tsiku;


Ndipo aphunziraponso kuchita ulesi, aderuderu; koma osati ulesi wokha, komatunso alankhula zopanda pake, nachita mwina ndi mwina, olankhula zosayenera.


kuti musakhale aulesi, koma akuwatsanza iwo amene alikulowa malonjezano mwa chikhulupiriro ndi kuleza mtima.