Ahebri 6:12 - Buku Lopatulika12 kuti musakhale aulesi, koma akuwatsanza iwo amene alikulowa malonjezano mwa chikhulupiriro ndi kuleza mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 kuti musakhale aulesi, koma akuwatsanza iwo amene alikulowa malonjezano mwa chikhulupiriro ndi kuleza mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Sitifuna kuti mukhale aulesi, koma kuti mutsanzire anthu amene, pakukhulupirira ndi pakupirira, akulandira zimene Mulungu adalonjeza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ife sitikufuna kuti inu mukhale aulesi, koma mutsatire anthu amene, pokhulupirira ndi kupirira, akulandira zimene zinalonjezedwa. Onani mutuwo |