Ahebri 6:11 - Buku Lopatulika11 Koma tikhumba kuti yense wa inu aonetsere changu chomwechi cholinga kuchiyembekezo chokwanira kufikira chitsiriziro; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Koma tikhumba kuti yense wa inu aonetsere changu chomwechi cholinga kuchiyembekezo chokwanira kufikira chitsiriziro; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tikufunitsitsa kuti aliyense mwa inu apitirire kuwonetsa changu chomwechi mpaka potsiriza, kuti chiyembekezo chanu chifike pake penipeni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ife tikufuna kuti aliyense wa inu aonetse changu chomwechi mpaka kumapeto, kuti zichitikedi zomwe mukuyembekezera. Onani mutuwo |