Mateyu 20:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo pamene adapangana ndi antchito, pa rupiya latheka limodzi tsiku limodzi, anawatumiza kumunda wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo pamene adapangana ndi antchito, pa rupiya latheka limodzi tsiku limodzi, anawatumiza kumunda wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adaapangana nawo kuti adzaŵalipira ndalama imodzi yasiliva pa tsiku, naŵatuma kumunda kwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Anagwirizana kuwalipira dinari monga malipiro a tsiku limodzi ndipo anawatumiza mʼmunda wake wamphesa. Onani mutuwo |