Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 15:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo panali ora lachitatu, ndipo anampachika Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo panali ora lachitatu, ndipo anampachika Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Pamene adampachika pa mtanda, nkuti nthaŵi ili 9 koloko m'maŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Linali ora lachitatu mmawa pamene anamupachika Yesu.

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:25
6 Mawu Ofanana  

Ndipo ora lachisanu ndi chimodzi panali mdima padziko lonse, kufikira ora lachisanu ndi chinai.


Ndipo pofika ora lachisanu ndi chimodzi, panali mdima padziko lonse, kufikira ora lachisanu ndi chinai.


Ndipo pa ora lachisanu ndi chinai Yesu anafuula ndi mau okweza, Eloi, Eloi, lama sabakitani? ndiko kusandulika, Mulungu wanga, Mulungu wanga mwandisiyiranji Ine?


Ndipo ora lake pamenepo linali ngati lachisanu ndi chimodzi. Ndipo panali mdima padziko lonse kufikira ora lachisanu ndi chinai, ndipo dzuwa linada.


Koma linali tsiku lokonza Paska; panali monga ora lachisanu ndi chimodzi. Ndipo ananena kwa Ayuda, Taonani, mfumu yanu!


Pakuti awa sanaledzere monga muyesa inu; pakuti ndi ora lachitatu lokha la tsiku;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa