Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 2:15 - Buku Lopatulika

15 Pakuti awa sanaledzere monga muyesa inu; pakuti ndi ora lachitatu lokha la tsiku;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Pakuti awa sanaledzera monga muyesa inu; pakuti ndi ora lachitatu lokha la tsiku;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Anthuŵa sadaledzere ai, monga mukuganizira inu, pakuti nthaŵi idakali 9 koloko m'maŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Kunena zoona, anthu awa sanaledzere ayi, monga momwe mukuganizira, pakuti ino ndi 9 koloko mmawa!

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 2:15
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anatuluka dzuwa litakwera, naona ena ataima chabe pabwalo;


nanena naye, Munthu aliyense amayamba kuika vinyo wokoma; ndipo anthu atamwatu, pamenepo wina wosakoma; koma iwe wasunga vinyo wokoma kufikira tsopano lino.


komatu ichi ndi chimene chinanenedwa ndi mneneri Yowele,


Ndipo Hana anayankha, nati, Iai, mbuyanga. Ine ndili mkazi wa mtima wachisoni; sindinamwe vinyo kapena chakumwa chowawa, koma ndinatsanulira mtima wanga pamaso pa Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa