Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 17:7 - Buku Lopatulika

Ndipo Yesu anadza, nawakhudza nati, Ukani, musaopa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yesu anadza, nawakhudza nati, Ukani, musaopa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Yesu adabwera, naŵakhudza nkunena kuti, “Dzukani, musachite mantha.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Yesu anabwera nawakhudza nati, “Dzukani, musaope.”

Onani mutuwo



Mateyu 17:7
10 Mawu Ofanana  

Ndipo taonani, linandikhudza dzanja ndi kundikhalitsa ndi maondo anga, ndi zikhato za manja anga.


Pamenepo anandikhudzanso wina, maonekedwe ake ngati munthu, nandilimbikitsa ine.


Ndipo m'mene analikulankhula ndi ine ndinagwidwa ndi tulo tatikulu, nkhope yanga pansi; koma anandikhudza, nandiimiritsa pokhala inepo.


inde pakunena ine m'kupemphera, munthu uja Gabriele, amene ndidamuona m'masomphenya poyamba paja, anauluka mwaliwiro nandikhudza ngati nthawi yakupereka nsembe ya madzulo.


Koma pomwepo Yesu analankhula nao, nati, Limbani mtima; ndine; musaope.


Ndipo pamene ophunzira anamva, anagwa nkhope zao pansi, naopa kwakukulu.


Ndipo iwo, pokweza maso ao sanaone munthu, koma Yesu yekha.


ndipo m'mene anakhala ndi mantha naweramira pansi nkhope zao, anati kwa iwo, Mufuniranji wamoyo pa akufa?


komatu, uka, nulowe m'mzinda, ndipo kudzanenedwa kwa iwe chimene uyenera kuchita.


Ndipo pamene ndinamuona Iye, ndinagwa pa mapazi ake ngati wakufa; ndipo anaika dzanja lake lamanja pa ine, nati, Usaope, Ine ndine Woyamba ndi Wotsiriza,