Danieli 10:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo taonani, linandikhudza dzanja ndi kundikhalitsa ndi maondo anga, ndi zikhato za manja anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo taonani, linandikhudza dzanja ndi kundikhalitsa ndi maondo anga, ndi zikhato za manja anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Dzanja linandikhudza ndi kundinyamula ndipo ndinachita ngati kuwerama pa mawondo manja atagwira pansi. Onani mutuwo |