Mateyu 14:27 - Buku Lopatulika27 Koma pomwepo Yesu analankhula nao, nati, Limbani mtima; ndine; musaope. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Koma pomwepo Yesu analankhula nao, nati, Limbani mtima; ndine; musaope. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Koma nthaŵi yomweyo Yesu adaŵauza kuti, “Khazikani mtima pansi, ndine; musaope.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Koma Yesu nthawi yomweyo anawawuza kuti, “Limbani mtima! Ndine, musaope.” Onani mutuwo |