Mateyu 17:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo iwo, pokweza maso ao sanaone munthu, koma Yesu yekha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo iwo, pokweza maso ao sanaone munthu, koma Yesu yekha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Iwo aja poŵeramuka, adangoona kuti palibe munthu winanso, koma Yesu yekha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Atayangʼana, sanaone wina aliyense kupatula Yesu yekha. Onani mutuwo |