Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 17:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo Yesu anadza, nawakhudza nati, Ukani, musaopa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo Yesu anadza, nawakhudza nati, Ukani, musaopa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Koma Yesu adabwera, naŵakhudza nkunena kuti, “Dzukani, musachite mantha.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Ndipo Yesu anabwera nawakhudza nati, “Dzukani, musaope.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 17:7
10 Mawu Ofanana  

Ndipo taonani, linandikhudza dzanja ndi kundikhalitsa ndi maondo anga, ndi zikhato za manja anga.


Pamenepo anandikhudzanso wina, maonekedwe ake ngati munthu, nandilimbikitsa ine.


Ndipo m'mene analikulankhula ndi ine ndinagwidwa ndi tulo tatikulu, nkhope yanga pansi; koma anandikhudza, nandiimiritsa pokhala inepo.


inde pakunena ine m'kupemphera, munthu uja Gabriele, amene ndidamuona m'masomphenya poyamba paja, anauluka mwaliwiro nandikhudza ngati nthawi yakupereka nsembe ya madzulo.


Koma pomwepo Yesu analankhula nao, nati, Limbani mtima; ndine; musaope.


Ndipo pamene ophunzira anamva, anagwa nkhope zao pansi, naopa kwakukulu.


Ndipo iwo, pokweza maso ao sanaone munthu, koma Yesu yekha.


ndipo m'mene anakhala ndi mantha naweramira pansi nkhope zao, anati kwa iwo, Mufuniranji wamoyo pa akufa?


komatu, uka, nulowe m'mzinda, ndipo kudzanenedwa kwa iwe chimene uyenera kuchita.


Ndipo pamene ndinamuona Iye, ndinagwa pa mapazi ake ngati wakufa; ndipo anaika dzanja lake lamanja pa ine, nati, Usaope, Ine ndine Woyamba ndi Wotsiriza,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa