Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 16:7 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo anafunsana wina ndi mnzake, nati, Sitinatenge mikate.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo anafunsana wina ndi mnzake, nati, Sitinatenga mikate.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo ophunzirawo adayamba kukambirana nkumati, “Akuterotu chifukwa sitidatenge buledi.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anakambirana pakati pawo za izi ndipo anati, “Ichi nʼchifukwa chakuti sitinatenge buledi aliyense.”

Onani mutuwo



Mateyu 16:7
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anati kwa iwo, Yang'anirani mupewe chotupitsa mkate cha Afarisi ndi Asaduki.


Koma Yesu, m'mene anadziwa, anati, Ha, inu okhulupirira pang'ono, mufunsana chifukwa ninji wina ndi mnzake, kuti simunatenga mikate?


Ubatizo wa Yohane, uchokera kuti? Kumwamba kodi kapena kwa anthu? Koma iwo anafunsana wina ndi mnzake, kuti, Tikati, Kumwamba, Iye adzati kwa ife, Munalekeranji kumvera iye?


Ndipo anasunga mauwo, nafunsana mwa iwo okha, kuti, Kuuka kwa akufa nchiyani?


Ndipo kunali m'kukambirana kwao ndi kufunsana, Yesu mwini anayandikira, natsagana nao.


Ndipo anayamba kutsutsana kuti wamkulu mwa iwo ndani.


Koma Petro anati, Iaitu, Mbuye; pakuti sindinadye ine ndi kale lonse kanthu wamba ndi konyansa.