Marko 9:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo anasunga mauwo, nafunsana mwa iwo okha, kuti, Kuuka kwa akufa nchiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo anasunga mauwo, nafunsana mwa iwo okha, kuti, Kuuka kwa akufa nchiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Iwo adasungadi chinsinsichi, koma ankafunsana okhaokha kuti, “Kodi kuuka kwa akufa akunena Yesuku ndiye kuti chiyani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Iwo anayisunga nkhaniyo nakambirana za tanthauzo lake la “Kuuka kwa akufa.” Onani mutuwo |