Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 9:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo anasunga mauwo, nafunsana mwa iwo okha, kuti, Kuuka kwa akufa nchiyani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo anasunga mauwo, nafunsana mwa iwo okha, kuti, Kuuka kwa akufa nchiyani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Iwo adasungadi chinsinsichi, koma ankafunsana okhaokha kuti, “Kodi kuuka kwa akufa akunena Yesuku ndiye kuti chiyani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Iwo anayisunga nkhaniyo nakambirana za tanthauzo lake la “Kuuka kwa akufa.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 9:10
15 Mawu Ofanana  

Ndipo abale ake anamchitira iye nsanje, koma atate wake anasunga mau amene m'mtima mwake.


Ndipo Petro anamtenga Iye, nayamba kumdzudzula, kuti, Dzichitireni chifundo, Ambuye; sichidzatero kwa Inu ai.


Ndipo anamfunsa Iye, nanena, Nanga alembi anena kuti adzayamba kufika Eliya?


Koma iwo sanazindikire mauwo, naopa kumfunsa.


Ndipo pakutsika iwo paphiri, Iye anawalamula kuti asauze munthu zinthu zimene adaziona, koma pamene Mwana wa Munthu akadzauka kwa akufa.


Izi sanazidziwe ophunzira ake poyamba; koma pamene Yesu analemekezedwa, pamenepo anakumbukira kuti izi zinalembedwa za Iye, ndi kuti adamchitira Iye izi.


Ndipo akukonda nzeru ena a Epikurea ndi a Stoiki anatengana naye. Ena anati, Ichi chiyani afuna kunena wobwetuka uyu? Ndipo ena, Anga wolalikira ziwanda zachilendo, chifukwa analalikira Yesu ndi kuuka kwa akufa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa