Marko 9:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo pakutsika iwo paphiri, Iye anawalamula kuti asauze munthu zinthu zimene adaziona, koma pamene Mwana wa Munthu akadzauka kwa akufa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo pakutsika iwo paphiri, Iye anawalamula kuti asauze munthu zinthu zimene adaziona, koma pamene Mwana wa Munthu akadzauka kwa akufa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Pamene ankatsika phirilo, Yesu adaŵaletsa kuti zimene adaaonazo asauze wina aliyense mpaka Mwana wa Munthu atauka kwa akufa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Pamene ankatsika kuchokera ku phiri, Yesu anawalamulira kuti asawuze aliyense zimene anaona mpaka Mwana wa Munthu atauka kwa akufa. Onani mutuwo |