Marko 9:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo dzidzidzi pounguzaunguza, sanapenye munthu wina yense, koma Yesu yekha, ndi iwo eni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo dzidzidzi pounguzaunguza, sanapenye munthu wina yense, koma Yesu yekha, ndi iwo eni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Mwadzidzidzi ophunzirawo poyang'anayang'ana, adangoona kuti palibenso wina amene anali nawo pamenepo, koma Yesu yekha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mwadzidzidzi, atayangʼanayangʼana, sanaonenso wina aliyense ali ndi iwo kupatula Yesu. Onani mutuwo |