Machitidwe a Atumwi 10:14 - Buku Lopatulika14 Koma Petro anati, Iaitu, Mbuye; pakuti sindinadye ine ndi kale lonse kanthu wamba ndi konyansa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma Petro anati, Iaitu, Mbuye; pakuti sindinadya ine ndi kale lonse kanthu wamba ndi konyansa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma Petro adati, “Iyai, pepani Ambuye, ine sindinadyepo ndi kale lonse chinthu chosayera kapena chonyansa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Petro anayankha kuti, “Ayi, Ambuye! Ine sindinadyepo kanthu kosayeretsedwa kapena konyansa.” Onani mutuwo |