Luka 24:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo kunali m'kukambirana kwao ndi kufunsana, Yesu mwini anayandikira, natsagana nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo kunali m'kukambirana kwao ndi kufunsana, Yesu mwini anayandikira, natsagana nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Akukambirana choncho nkumafunsana, Yesu mwiniwake adayandikira nkumatsagana nawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Pamenepo Yesu mwini wake anabwera ndi kuyenda nawo pamodzi; Onani mutuwo |