Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 13:9 - Buku Lopatulika

Amene ali ndi makutu, amve.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Amene ali ndi makutu, amve.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Yesu adati, “Amene ali ndi makutu, amve!”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amene ali ndi makutu amve.”

Onani mutuwo



Mateyu 13:9
14 Mawu Ofanana  

Amene ali ndi makutu akumva, amve.


Ndipo ophunzirawo anadza, nati kwa Iye, Chifukwa chanji muphiphiritsira iwo m'mafanizo?


Koma maso anu ali odala, chifukwa apenya; ndi makutu anu chifukwa amva.


Ngati munthu ali nao makutu akumva, amve.


Ndipo ananena, Amene ali nao makutu akumva amve.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Iye amene apambana sadzachitidwa choipa ndi imfa yachiwiri.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye wopambana, ndidzampatsa mana obisika, ndipo ndidzampatsa mwala woyera, ndi pamwalawo dzina latsopano lolembedwapo, wosalidziwa munthu aliyense koma iye wakuulandira.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye amene apambana ndidzampatsa kudya za ku mtengo wa moyo umene uli mu Paradaiso wa Mulungu.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.