Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 81:13 - Buku Lopatulika

Ha! Akadandimvera anthu anga, akadayenda m'njira zanga Israele!

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ha! Akadandimvera anthu anga, akadayenda m'njira zanga Israele!

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Anthu anga akadandimvera, Aisraele akadayenda m'njira zanga,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Anthu anga akanangondimvera, Israeli akanatsatira njira zanga,

Onani mutuwo



Masalimo 81:13
8 Mawu Ofanana  

momwemo adzadya zipatso za mayendedwe ao, nadzakhuta zolingalira zao.


Mwenzi utamvera malamulo anga mtendere wako ukanakhala ngati mtsinje, ndi chilungamo chako monga mafunde a nyanja;


Koma sanamvere, sanatchere khutu, koma anayenda mu upo ndi m'kuuma kwa mtima wao woipa, nabwerera chambuyo osayenda m'tsogolo.


Ha, Yerusalemu, Yerusalemu, amene umapha aneneri, ndi kuwaponya miyala iwo otumidwa kwa iwe! Ine ndinafuna kangati kusonkhanitsa pamodzi ana ako, inde monga thadzi lisonkhanitsa anapiye ake m'mapiko ake, koma inu simunafune ai!


Akadakhala nazo nzeru, akadazindikira ichi, akadasamalira chitsirizo chao!


Ha? Mwenzi akadakhala nao mtima wotere wakundiopa Ine, ndi kusunga malamulo anga masiku onse, kuti chiwakomere iwo ndi ana ao nthawi zonse!