Masalimo 81:12 - Buku Lopatulika12 Potero ndinawaperekera kuuma mtima kwao, ayende monga mwa uphungu waowao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Potero ndinawaperekera kuuma mtima kwao, ayende monga mwa uphungu waowao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Choncho ndidaŵasiya ndi mitima yao yosamverayo, kuti atsate zimene ankafuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Kotero ndinawasiya ndi mitima yawo yosamverayo kuti atsate zimene ankafuna. Onani mutuwo |