Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 81:11 - Buku Lopatulika

11 Koma anthu anga sanamvere mau anga; ndipo Israele sanandivomere.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Koma anthu anga sanamvere mau anga; ndipo Israele sanandivomere.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 “Koma anthu anga sadamvere mau anga. Israele adandinyoza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 “Koma anthu anga sanandimvere; Israeli sanandigonjere.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 81:11
16 Mawu Ofanana  

Pamenepo anati, Kabwereke zotengera kwina kwa anansi ako onse, zotengera zopanda kanthu, zisakhale pang'ono.


Ndipo Mose ndi Aroni ananena ndi ana onse a Israele, Madzulo mudzadziwa kuti Yehova anakutulutsani m'dziko la Ejipito;


Ine ndine Yehova Mulungu wako, amene ndinatulutsa iwe ku dziko la Ejipito, kunyumba ya ukapolo.


Koma pamene anaona kuti Mose anachedwa kutsika m'phiri, anthuwo anasonkhana kwa Aroni, nanena naye, Ukani, tipangireni milungu yakutitsogolera; pakuti Mose uyu, munthuyu anatikweza kuchokera m'dziko la Ejipito, sitidziwa chomwe chamgwera.


Chifukwa chake nena kwa ana a Israele Ine ndine Yehova, ndipo ndidzakutulutsani pansi pa akatundu a Aejipito ndipo ndidzakulanditsani ku ukapolo wanu; ndipo ndidzakuombolani ndi dzanja lotambasuka, ndi maweruzo aakulu;


anakana uphungu wanga, nanyoza kudzudzula kwanga konse;


Chifukwa chake, taonani, masiku adza, ati Yehova, kuti sadzanenanso, Pali Yehova, amene anakweza ana a Israele kuwatulutsa m'dziko la Ejipito.


Koma anakana kumvera, nakaniza phewa lao, natseka makutu ao, kuti asamve.


ndipo pofika, uipeza yosesa ndi yokonzeka.


Koma Yesuruni anasanduka wonenepa, natazira; wasanduka wonenepa, wakula, wakuta ndi mafuta; pamenepo anasiya Mulungu amene anamlenga, napeputsa thanthwe la chipulumutso chake.


Mwaleka Thanthwe limene linakubalani, mwaiwala Mulungu amene anakulengani.


Ine ndine Yehova Mulungu wako amene ndinakutulutsa m'dziko la Ejipito, m'nyumba ya ukapolo.


ndipo mutani, kulanga koposa kotani nanga adzayesedwa woyenera iye amene anapondereza Mwana wa Mulungu, nayesa mwazi wa chipangano umene anayeretsedwa nao chinthu wamba, nachitira chipongwe Mzimu wa chisomo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa