Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 8:8 - Buku Lopatulika

mbalame za m'mlengalenga, ndi nsomba za m'nyanja. Zopita m'njira za m'nyanja.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

mbalame za m'mlengalenga, ndi nsomba za m'nyanja. Zopita m'njira za m'nyanja.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

mbalame zamumlengalenga, nsomba zam'nyanja, ndi zonse zoyenda pansi pa nyanja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

mbalame zamlengalenga ndi nsomba zamʼnyanja zonse zimene zimayenda pansi pa nyanja.

Onani mutuwo



Masalimo 8:8
4 Mawu Ofanana  

Kodi ukhoza kusakira mkango waukazi nyama? Ndi kukwaniritsa chakudya cha misona,


Tapenya tsono mvuu ndinaipanga pamodzi ndi iwe, ikudya udzu ngati ng'ombe.


Nyama zakuthengo ndi zoweta zonse; zokwawa, ndi mbalame zakuuluka.