Masalimo 8:9 - Buku Lopatulika9 Yehova, Ambuye wathu, dzina lanu liposadi nanga padziko lonse lapansi! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Yehova, Ambuye wathu, dzina lanu liposadi nanga pa dziko lonse lapansi! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chauta, Ambuye athu, dzina lanu ndi lotchuka pa dziko lonse lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Inu Yehova, Ambuye athu, dzina lanu ndi lamphamvudi pa dziko lonse lapansi! Onani mutuwo |